LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/15 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 14

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 14
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA DECEMBER 14
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 12/15 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa December 14

MLUNGU WA DECEMBER 14

Nyimbo 50 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

ia mutu 4 ndime 16-31, ndi kubwelelamo pa tsa. 41 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 2 Mbiri 15-19 (Mph. 8)

Na. 1: 2 Mbiri 16:1-9 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Dziko la Akasidi Linali Kuti, Nanga Akasidi Anali Ndani? (Mph. 5)

Na. 3: Esau—Mutu: Zosankha Zathu Zimaonetsa Kuti Timayamikila Zinthu Zopatulika—w13 5/15 tsa. 27-28 ndime 6-11 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: “Tiyenela kukumana ndi masautso ambili kuti tikaloŵe mu Ufumu wa Mulungu.”—Machitidwe 14:22.

Nyimbo 128

Mph.30: “Yendani mwa Cikhulupililo, Osati mwa Zooneka ndi Maso.” Mafunso ndi mayankho. Gwilitsani nchito mfundo za m’ndime yoyamba ndi yomaliza monga mau oyamba ndi omaliza. Ngati n’zosatheka kuonelela vidiyo, kambilanani mwa mafunso ndi mayankho nkhani yakuti “Yendani mwa Cikhulupililo, Osati mwa Zooneka ndi Maso,” mu Nsanja ya Olonda ya September 15, 2005 tsamba 16-20.

Nyimbo 133 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani