LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 January tsa. 3
  • Kulambila Koona Kumafuna Kugwila Nchito Mwakhama

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kulambila Koona Kumafuna Kugwila Nchito Mwakhama
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Mulungu Athandiza Mfumu Hezekiya
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Kodi Abusa 7 Ndi Atsogoleli 8 Ndani Masiku Ano?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • “Inu Mulungu Wanga, Cikhulupililo Canga Cili mwa Inu”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 January tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | 2 MBIRI 29–32

Kulambila Koona Kumafuna Kugwila Nchito Mwakhama

Yopulinta
Kacisi wa Solomo ku Yerusalemu

Hezekiya abwezeletsa kulambila koona molimba mtima

29:10-17

  • 746-716 B.C.E.

    Ulamulilo wa Hezekiya

  • NISANI 746 B.C.E.

    • Tsiku loyamba mpaka la 8: Kuyeletsa bwalo lamkati

    • Tsiku la 9 mpaka la 16: Kuyeletsa nyumba ya Yehova

    • Kuphimba macimo a Aisiraeli onse ndiponso kubwezeletsa kulambila koona zinayamba

  • 740 B.C.E

    Kugonjetsedwa kwa Mzinda wa Samariya

Hezekiya aitana anthu onse a mtima wabwino kuti adzalambile Mulungu

30:5, 6, 10-12

  • Asilikali othamanga anatumidwa kukapeleka makalata olengeza za Pasika m’madela onse a dzikolo kuyambila ku Beere-seba mpaka ku Dani

  • Anthu ena anali kunyoza, koma ambili analandila uthengawo mwacisangalalo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani