LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 January tsa. 4
  • Yehova Amaona Munthu Wolapa ndi Mtima Wonse Kukhala Wamtengo Wapatali

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova Amaona Munthu Wolapa ndi Mtima Wonse Kukhala Wamtengo Wapatali
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Yosiya Anali Kukonda Cilamulo ca Mulungu
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Maguwa Ansembe a pa Cihema Komanso Nchito Yawo pa Kulambila Koona
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Mfumu Yabwino Yotsilizila Ya Isiraeli
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 January tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | 2 MBIRI 33–36

Yehova Amaona Munthu Wolapa ndi Mtima Wonse Kukhala Wamtengo Wapatali

Yopulinta

MANASE

Yehova analola kuti agwidwe ndi Asuri ndipo anapita naye ku Babulo m’matangadza

Mfumu Manase

ULAMULILO WAKE ASANATENGEDWE KU UKAPOLO

  • Anamangila milungu yonama maguwa ansembe

  • Anapeleka ana ake nsembe

  • Anakhetsa magazi a anthu osalakwa

  • Analimbikitsa anthu onse kucita zamatsenga

ULAMULILO WAKE ATAMASULIDWA

  • Anadzicepetsa kwambili

  • Anapemphela kwa Yehova; ndipo anapeleka nsembe

  • Anacotsa maguwa a nsembe a milungu yonama

  • Analimbikitsa anthu onse kutumikila Yehova

YOSIYA

Mfumu Yosiya

ULAMULILO WAKE WONSE

  • Anafunafuna Yehova

  • Anayeletsa Yuda ndi Yerusalemu

  • Anakonza nyumba ya Yehova; anapeza buku la Cilamulo ca Yehova

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani