LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 October tsa. 7
  • Maguwa Ansembe a pa Cihema Komanso Nchito Yawo pa Kulambila Koona

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maguwa Ansembe a pa Cihema Komanso Nchito Yawo pa Kulambila Koona
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Zimene Tingaphunzile pa Zocitika za pa Tsiku la Mwambo Wophimba Macimo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Mfundo Zimene Tingaphunzile mu Buku la Levitiko
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Yamikilani Mwayi Wanu Wolambila Yehova M’kacisi Wake Wauzimu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Cihema Colambililako
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 October tsa. 7
Nsalu yophimba cihema yayanzulidwa kuti mkati na mmene anacipangila zionekele. Pafupi pake pali beseni yamkuwa na guwa la nsembe zopseleza.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKSODO 37–38

Maguwa Ansembe a pa Cihema Komanso Nchito Yawo pa Kulambila Koona

37:25, 29; 38:1

Maguwa ansembe a pa cihema anamangidwa motsatila malangizo amene Yehova anapeleka, ndipo anali na tanthauzo lapadela.

  • Guwa la nsembe zofukiza.

    Mofanana na fungo la zofukiza zosakanizidwa mwaluso, mapemphelo opelekedwa na atumiki a Yehova amam’kondweletsa iye

  • Guwa la nsembe zopseleza.

    Yehova anali kulandila nsembe zopelekedwa pa guwa lansembe zopseleza. Guwali linali kukhala kutsogolo kwa malo opatulika. Izi zitikumbutsa kuti kukhulupilila nsembe ya dipo la Yesu n’kofunika kwambili kuti tiyanjidwe na Mulungu.—Yoh. 3:16-18; Aheb. 10:5-10

Kodi tingawakonze bwanji mapemphelo athu monga zofukiza pamaso pa Mulungu?—Sal. 141:2

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani