LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 February tsa. 5
  • Olambila Okhulupilika Amacilikiza Dongosolo la Gulu la Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Olambila Okhulupilika Amacilikiza Dongosolo la Gulu la Mulungu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Nehemiya anali woyang’anila wa citsanzo cabwino kwambili
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Mwapatulidwa
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 February tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | NEHEMIYA 9–11

Olambila Okhulupilika Amacilikiza Dongosolo la Gulu la Mulungu

Banja laciisraeli likucita Cikondwelelo ca Misasa

Anthu a Mulungu anacilikiza kulambila koona ndi mtima wonse m’njila zambili

10:28-30, 32-39; 11:1, 2

  • Aisiraeli anakonzekela ndi kucita Cikondwelelo ca Misasa m’njila yoyenelela.

  • Anthu anali kusonkhana tsiku lililonse kuti amvetsele Cilamulo ca Mulungu cikamaŵelengedwa, ndipo anali kusangalala kwambili.

  • Anthu anali kulapa macimo ao ndi kupemphela kuti Yehova awadalitse.

  • Anthu anavomeleza kucilikiza dongosolo la gulu la Mulungu.

Kucilikiza dongosolo la gulu la Mulungu kunali kuphatikizapo:

  • Mwamuna ndi mkazi wake ndipo onse amalambila Yehova

    Kumanga banja ndi anthu okhawo amene anali kulambila Yehova

  • Makobidi aŵili

    Kupeleka ndalama

  • Mpukutu wa Cilamulo ca Mose

    Kusunga Sabata

  • Nkhuni za paguwa lansembe

    Kupeleka nkhuni ku guwa lansembe

  • Zipatso zoyambilila kuca, ndiponso mwana wa nkhosa wamphongo woyamba kubadwa

    Kupeleka zipatso zoyambilila kuca, ndi mwana woyamba kubadwa wa nyama iliyonse kwa Yehova

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani