LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 March tsa. 3
  • Esitere Anaimila Yehova ndi Anthu Ake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Esitere Anaimila Yehova ndi Anthu Ake
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Esitere Apulumutsa Anthu a Mtundu Wake
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Mordekai Ndi Estere
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 March tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | ESITERE 6-10

Esitere Anaimila Yehova ndi Anthu Ake

Yopulinta

Esitere anali wolimba mtima ndiponso woganizila ena poimila Yehova ndi anthu ake

8:3-5, 9

  • Esitere ndi Moredekai anali otetezeka. Koma lamulo la Hamani lonena kuti Ayuda onse aphedwe, linali kulengezedwabe m’madela onse a ufumuwo

  • Kaciŵilinso, Esitere anaika moyo wake paciswe n’kukaonekela pamaso pa mfumu asanaitanidwe. Iye analila ndi kucondelela mfumu kuti isinthe ciwembu cimene Hamani anakonzela Ayuda

  • Malamulo amene mfumu yakhazikitsa sanali kusinthidwa. Conco, mfumu inapatsa mphamvu Esitere ndi Moredekai yakuti akhazikitse lamulo lina latsopano

Yehova anathandiza kwambili anthu ake kuti apambane

8:10-14, 17

  • Lamulo latsopano lopatsa Ayuda ufulu wodziteteza linakhazikitsidwa

  • Anthu okwela pamahachi anatumizidwa m’zigawo zonse za ufumuwo, ndipo Ayuda anayamba kukonzekela nkhondo

  • Anthu ambili anaona kuti Mulungu anateteza anthu ake, ndipo io analoŵa Ciyuda

Esitere akuyang’ana Moredekai amene akuuza mlembi wake kuti alembe lamulo latsopano
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani