LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 December tsa. 4
  • Ulosi wa Mesiya Umene Unakwanilitsika

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ulosi wa Mesiya Umene Unakwanilitsika
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 December tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YESAYA 6-10

Ulosi wa Mesiya Umene Unakwanilitsika

Yopulinta

Zaka zambili Yesu akalibe kubadwa, Yesaya analosela kuti Mesiya akayamba kulalikila “m’cigawo ca Yorodano, ku Galileya kumene kunali kukhala anthu a mitundu ina.” Yesu anakwanilitsa ulosiwu pamene anali kuyenda m’Galileya monse kulalikila uthenga wabwino.—Yes. 9:1, 2.

Mapu a Galileya
  • Mtsuko wa vinyo

    Anacita cozizwitsa coyamba—Yoh. 2:1-11 (ku Kana)

  • Atumwi 12

    Anasankha atumwi ake—Maliko 3:13, 14 (pafupi na Kaperenao)

  • Yesu aphunzitsa

    Analalikila pa phili—Mat. 5:1–7:27 (pafupi na Kaperenao)

  • Wacicepele waukitsidwa

    Anaukitsa mwana mmodzi yekha wa mayi wamasiye—Luka 7:11-17 (ku Naini)

  • Yesu aonekela kwa ophunzila ake ataukitsiwa

    Anaonekela kwa ophunzila ake 500 pambuyo poukitsidwa—1 Akor. 15:6 (ku Galileya)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani