LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsa. 7
  • May 29–June 4

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • May 29–June 4
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 May tsa. 7

May 29–June 4

YEREMIYA 49-50

  • Nyimbo 102 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 mineti kapena kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Yehova Amadalitsa Odzicepetsa ndi Kulanga Odzitukumula”: (10 min.)

    • Yer. 50:4-7—Aisiraeli olapa ndi odzicepetsa amene anatsalapo, anali kudzamasulidwa mu ukapolo ndi kubwelela ku Ziyoni

    • Yer. 50:29-32—Babulo anali kudzawonongedwa cifukwa codzitukumula pamaso pa Yehova (it-1 peji 54)

    • Yer. 50:38, 39—Anati ku Babulo sikudzakhalanso anthu (jr peji 161 pala. 15; w98 4/1 peji 20 pala. 20)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Yer. 49:1, 2—N’cifukwa ciani Aamoni anadzudzulidwa ndi Yehova? (it-1 peji 94 pala. 6)

    • Yer. 49:17, 18—Kodi Edomu anakhala bwanji monga Sodomu na Gomora? Ndipo n’cifukwa ciani? (jr peji 163 pala. 18; ip-2 peji 351 pala. 6)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 mineti kapena kucepelapo) Yer. 50:1-10

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 mineti kapena kucepelapo) T-32—Yalani maziko a ulendo wobwelelako.

  • Ulendo Wobwelelako: (4 mineti kapena kucepelapo) T-32—Kambilanani mbali yakuti “Ganizilani Funso Ili.” Yalani maziko a ulendo wotsatila.

  • Nkhani: (6 mineti kapena kucepelapo) w15 3/15 peji 17—Mutu Wake: M’zaka Zapitazi, N’cifukwa Ninji Mabuku Athu Sakambapo Kaŵili-kaŵili za Zinthu Zocitila Mthunzi ndi Zocitilidwa Mthunzi?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 56

  • Cotsani Mtanda wa Denga: (15 min.) Tambitsani vidiyo yakuti Cotsani Mtanda wa Denga (yendani ku mavidiyo BAIBULO). Ndiyeno kambilanani mafunso aya: Kodi m’bale anaonetsa bwanji mzimu wonyada ndi wosuliza? Cinam’thandiza n’ciani kusintha kaganizidwe kake? Nanga anapindula bwanji?

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) kr nkhani 13 mapa. 11-23

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 131 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani