LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsa. 7
  • Yehova Amadalitsa Odzicepetsa ndi Kulanga Odzitukumula

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova Amadalitsa Odzicepetsa ndi Kulanga Odzitukumula
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Adzaweluza Aliyense Malinga na Nchito Zake
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Yehova Ananenelatu za Pangano Latsopano
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Kuitaniwa Kucoka mu Mdima
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • Yang’anani kwa Yehova Kuti Akuthandizeni Kupilila na Kukutonthozani
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 May tsa. 7

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YEREMIYA 49-50

Yehova Amadalitsa Odzicepetsa ndi Kulanga Odzitukumula

50:4-7

  • Aisiraeli olapa anagwetsa misozi ya cisangalalo pamene Yehova anawamasula mu ukapolo

  • Anakumbukilanso pangano lawo ndi iye na kuyenda ulendo wautali wobwelela ku Yerusalemu kukabwezeletsa kulambila koona

    Aisiraeli atuluka m’Babulo

50:29, 39

  • Ababulo odzikuzawo sanapulumuke cilango pocita nkhanza zaunkhalwe kwa anthu a Yehova

  • Monga mwa ulosi, Babulo anasanduka matongwe osakhalamo anthu

    Mwamuna wacibabulo wouma khosi, ndi matongwe a Babulo okhalamo nyama za kuchile
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani