LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsa. 5
  • Yehova Adzaweluza Aliyense Malinga na Nchito Zake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova Adzaweluza Aliyense Malinga na Nchito Zake
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Ebedi-meleki—Citsanzo ca Kulimba Mtima na Kukoma Mtima
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Yerusalemu Awonongedwa
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 May tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YEREMIYA 39-43

Yehova Adzaweluza Aliyense Malinga na Nchito Zake

Zedekiya sanamvele malangizo a Yehova akuti adzipeleke okha kwa a Babulo

39:4-7

  • Ana a Zedekiya anaphedwa iye akuona. Ndiyeno iye anabowoledwa maso, kumangidwa m’matangadza a unyolo, ndi kuponyedwa m’ndende ku Babulo mpaka imfa yake

    Mfumu Zedekiya anapandukila Yehova ndipo analangidwa mwa kubowoledwa maso ndi kumangidwa m’matangadza a unyolo

Ebedi-meleki anakhulupilila mwa Yehova ndi kudela nkhawa Yeremiya mneneli wa Mulungu

39:15-18

  • Yehova analonjeza kuti adzateteza Ebedi-meleki pa kuwonongedwa kwa Isiraeli

    Ebedi-meleki anafikila Zedekiya mopanda mantha ndiyeno sanaphedwe pamene Yerusalemu anali kuonongedwa

Yeremiya analalikila molimba mtima kwa zaka zambili Yerusalemu asanawonongedwe

40:1-6

  • Yehova anateteza Yeremiya pamene Yerusalemu anazingidwa, ndipo analinganiza kuti Ababulo am’masule

    Yeremiya alalikila mopanda mantha ndi kupatsidwa cakudya pamene Yerusalemu anazingidwa
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani