LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsa. 3
  • Ebedi-meleki—Citsanzo ca Kulimba Mtima na Kukoma Mtima

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ebedi-meleki—Citsanzo ca Kulimba Mtima na Kukoma Mtima
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Adzaweluza Aliyense Malinga na Nchito Zake
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Yehova Atumiza Yeremiya Kuti Akalalikile
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 May tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YEREMIYA 35-38

Ebedi-meleki—Citsanzo ca Kulimba Mtima na Kukoma Mtima

Ebedi-meleki, nduna ya m’bwalo la Mfumu Zedekiya, anaonetsa makhalidwe aumulungu

38:7-13

  • Ebedi-meleki afikila Mfumu Zedekiya

    Anacita zinthu molimba mtima ndi mwacangu mwa kukalankhula ndi Mfumu Zedekiya ndi kutulutsa Yeremiya m’citsime

  • Anaonetsanso kukoma mtima mwa kupatsa Yeremiya tuzidutswa twa nsalu kuti aike m’khwapa mwake kuti nthambo zisamuvulaze

    Yeremiya atulutsidwa m’citsime
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani