LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsa. 8
  • Kusamalila Malo Athu Olambilila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kusamalila Malo Athu Olambilila
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Tonse Tingatengeleko Mbali pa Kusamalila Malo Athu Olambilila
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Awa Ndi Malo Athu Olambilila
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Malo Olambilila
    Gulu Lokhazikitsidwa Kucita Cifunilo ca Yehova
  • Nchito Yomanga Imene Imalemekeza Yehova
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 May tsa. 8

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kusamalila Malo Athu Olambilila

Njila zothandizila kusamalila Nyumba za Ufumu: kupenta, kuyala kapeti, kuika za malaiti, ndi kucita copeleka ca ndalama

Nyumba zathu za Ufumu si Nyumba wamba; ni malo olambilila opelekedwa kwa Yehova. Kodi aliyense wa ife angathandize bwanji posamalila Nyumba ya Ufumu? Pambuyo potamba vidiyo yakuti Kusamalila Malo Athu Olambilila kambilanani mafunso aya.

  1. Kodi Nyumba za Ufumu zimagwila nchito yanji?

  2. N’cifukwa ciani tiyenela kusunga Nyumba yathu ya Ufumu ili yoyela ndi yokonzedwa bwino?

  3. N’ndani amasamalila nchito yokonza Nyumba ya Ufumu?

  4. N’cifukwa ciani kupewa ngozi n’kofunika? Nanga mu vidiyo mwaonamo zitsanzo zanji zopewela ngozi?

  5. Kodi tingalemekeze bwanji Yehova ndi zopeleka zathu?

N’DZAYAMBA KUTHANDIZILA MWA KUCITA IZI:

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani