LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 June tsa. 5
  • Ezekieli Anasangalala Polengeza Uthenga wa Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ezekieli Anasangalala Polengeza Uthenga wa Mulungu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Yehova Amatithandizila Kugwila Nchito Yolalikila
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 June tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | EZEKIELI 1-5

Ezekieli Anasangalala Polengeza Uthenga wa Mulungu

M’masomphenya, Yehova anapatsa Ezekieli mpukutu na kumuuza kuti adye mpukutuwo. Kodi zimenezi zinatanthauza ciani?

2:9–3:2

  • Ezekieli anafunika kuumvetsetsa uthenga wa Mulungu. Kusinkha-sinkha pa mau a mpukutuwo kunam’fika pamtima Ezekieli ndi kum’sonkhezela kulankhula

3:3

  • Mpukutuwo unali wonzuna cifukwa Ezekieli anali kuona utumiki wake moyenela

Atadya mpukutu woimila uthenga wa Mulungu, Ezekieli akamba ndi amuna a ku isiraeli

Kodi kupemphela na kucita phunzilo la Baibo, ndiponso kusinkha-sinkha kunganikhudze bwanji?

Ningacite ciani kuti niyambe kuona ulaliki moyenela?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani