LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 July tsa. 6
  • July 24-30

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • July 24-30
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 July tsa. 6

July 24-30

EZEKIELI 21-23

  • Nyimbo 99 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 mineti kapena kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Ufumuwo ni wa Uyo Ali Woyenelela Mwalamulo”: (10 min.)

    • Ezek. 21:25—“Mtsogoleli wa Isiraeli woipa” anali Mfumu Zedekiya (w07 7/1 peji 13 pala. 11)

    • Ezek. 21:26—Mzela wa mafumu ocokela mwa Davide olamulila mu Yerusalemu unali kudzatha (w11 8/15 peji 9 pala. 6)

    • Ezek. 21:27—Yesu Khristu ndiye “woyenelela mwalamulo” (w14 10/15 peji 10 pala. 14)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Ezek. 21:3—Kodi “lupanga” limene Yehova akusolola m’cimake n’ciani? (w07 7/1 peji 14 pala. 1)

    • Ezek. 23:49—Kodi mu caputa 23 akufotokozamo colakwa canji? Nanga titengapo phunzilo lanji? (w07 7/1 peji 14 pala. 6)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 mineti kapena kucepelapo) Ezek. 21:1-13

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 mineti kapena kucepelapo) fg—Chulani za vidiyo yakuti Kodi Phunzilo la Baibulo Limacitika Bwanji? na kukambilana (koma musawatambitse)

  • Ulendo Wobwelelako: (4 mineti kapena kucepelapo) bhs—Chulani ndi kukambilana za vidiyo (koma musawatambitse) yakuti Kodi Phunzilo la Baibulo Limacitika Bwanji? pokambilana ndi amene mumapelekela magazini.

  • Phunzilo la Baibo: (6 mineti kapena kucepelapo) bhs peji 217

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 93

  • “Tizionetsa Ulemu Tikafika pa Khomo la Munthu”: (15 min.) Nkhani yokambilana ya woyang’anila nchito. Yambani ndi kutambitsa vidiyo ya malangizo a mmene tingaonetsele ulemu tikafika pakhomo la munthu.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) kr nkhani 15 mapa. 18-28

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 29 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani