LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 August tsa. 4
  • August 14-20

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • August 14-20
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 August tsa. 4

August 14-20

EZEKIELI 32-34

  • Nyimbo 144 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 mineti kapena kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Udindo Waukulu wa Mlonda”: (10 min.)

    • Ezek. 33:7—Yehova anaika Ezekieli kukhala mlonda (it-2 peji 1172 pala. 2)

    • Ezek. 33:8, 9—Mlonda anali kupewa mlandu wa magazi mwa kucenjeza anthu (w88-E 1/1 peji 28 pala. 13)

    • Ezek. 33:11, 14-16—Yehova adzapulumutsa aja amene amamvela cenjezo (w12 3/15 peji 15 pala. 3)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Ezek. 33:32, 33—N’cifukwa ciani tifunika kulimbikilabe kulalikila olo kuti anthu akhale ndi mphwayi [kupanda cidwi]? (w91 3/15 peji 17 pala. 16-17)

    • Ezek. 34:23—Kodi lembali lakwanilitsika bwanji? (w07 4/1 peji 26 pala. 3)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 mineti kapena kucepelapo) Ezek. 32:1-16

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 mineti kapena kucepelapo) g17.4 nkhani ya pacikuto—Yalani maziko a ulendo wobwelelako.

  • Ulendo Wobwelelako: (4 mineti kapena kucepelapo) g17.4 nkhani ya pacikuto—Itanilani munthuyo kumisonkhano.

  • Phunzilo la Baibo: (6 min. kapena kucepelapo) fg phunzilo 2 mapa. 9-10—Onetsani mmene tingam’fikile pamtima wophunzila.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 67

  • “Kulitsani Makhalidwe Aumulungu—Kulimba Mtima: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Muzipewa Zinthu Zimene Zingakulepheletseni Kukhala Wokhulupilika—Kuopa Anthu.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) kr nkhani 16 mapa. 6-17

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 117 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani