LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 August tsa. 5
  • Udindo Waukulu wa Mlonda

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Udindo Waukulu wa Mlonda
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Yehova Amatithandizila Kugwila Nchito Yolalikila
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Ezekieli Anasangalala Polengeza Uthenga wa Mulungu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 August tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | EZEKIELI 32-34

Udindo Waukulu wa Mlonda

Alonda anali kukhala pa mpanda wa mzinda ndi m’nsanja zake kuti azicenjeza anthu za adani amene angabwele. Yehova anasankha Ezekieli kukhala “mlonda wa nyumba ya Isiraeli” wophiphilitsa.

Alonda anali kukhala pa mpanda wa mzinda
  • Alonda ali pa mpanda wa mzinda

    33:7

    Ezekieli anacenjeza Isiraeli kuti ciweluzo cidzabwela kwa iwo ngati sadzasiya njila zawo zoipa

    Nanga ise timalengeza uthenga wanji wocoka kwa Yehova?

  • Asilikali aloŵa cifukwa cakuti mlonda sanacenjeze anthu

    33:9, 14-16

    Mwa kucenjeza anthu, Ezekieli anapulumutsa moyo wake ndi wa anthu ena.

    N’ciani ciyenela kutituntha kulengeza mwacangu uthenga umene Yehova watipatsa?

Wiki ino nidzayesa kulalikila . . .

  • mnzanga wa m’kilasi

  • mnzanga wa ku nchito

  • m’bululu wanga amene si Mboni

  • anthu ena:

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani