LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 June tsa. 6
  • June 25–July 1

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • June 25–July 1
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 June tsa. 6

June 25–July 1

LUKA 4-5

  • Nyimbo 37 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Kanizani Ziyeso Mmene Yesu Anacitila” (10 min.)

    • Luka 4:1-4—Yesu sanagonje ku cilako-lako ca thupi (w13 8/1 peji 25 pala. 8)

    • Luka 4:5-8—Yesu sanatengeke na cilako-lako ca maso (w13 8/1 peji 25 pala. 10)

    • Luka 4:9-12—Yesu anakana kucita zinthu modzionetsela [Tambitsani vidiyo yopanda mau yakuti Pamwamba pa Cipupa ca Mpanda wa Kacisi.] (“Pamwamba pa Cipupa ca Mpanda wa Kacisi” nwtsty zithunzi; w13 8/1 peji 26 pala. 12)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Luka 4:17—N’ciani cionetsa kuti Yesu anali kuwadziŵa bwino Mau a Mulungu? (“mpukutu wa mneneri Yesaya” nwtsty mfundo younikila)

    • Luka 4:25—Kodi cilala cinatenga nthawi itali bwanji m’nthawi ya Eliya? (“zaka zitatu ndi miyezi 6” nwtsty mfundo younikila)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Luka 4:31-44

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Kubwelelako Kaciŵili: (3 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Ndiyeno, musiyileni kakhadi kongenela pa Webusaiti yathu.

  • Kubwelelako Kacitatu: (3 min. olo kucepelapo) Sankhani mwekha lemba na kugaŵila cofalitsa cophunzitsila Baibo.

  • Phunzilo la Baibo: (6 min. olo kucepelapo) jl phunzilo 28

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 28

  • “Pewani Misampha Poceza ndi Anthu pa Intaneti”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Muzisamala Poceza ndi Anthu pa Intaneti.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 26

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 105 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani