LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsa. 2
  • May 4-10

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • May 4-10
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 May tsa. 2

May 4-10

GENESIS 36-37

  • Nyimbo 114 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yosefe Anacitilidwa Nsanje” (10 min.)

    • Gen. 37:3, 4—Yosefe abale ake anali kumuzonda kwambili cifukwa atate ake anali kum’konda (w14 8/1 12-13)

    • Gen. 37:5-9, 11—Maloto a Yosefe anawonjezela nsanje ya abale ake (w14 8/1 13 ¶2-4)

    • Gen. 37:23, 24, 28—Nsanje inapangitsa abale ake a Yosefe kum’citila zinthu mwankhanza

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu

    • Gen. 36:1—N’cifukwa ciani Esau anapatsidwa dzina lina lakuti Edomu? (it-1 678)

    • Gen. 37:29-32—N’cifukwa ciani abale ake a Yosefe anaonetsa Yakobo mkanjo wa Yosefe umene unali wong’ambika komanso wamagazi? (it-1 561-562)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova Mulungu, ulaliki, kapena mbali ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Gen. 36:1-19 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa: (10 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Muzikamba Zosavuta Kumvetsa, ndiyeno kambilanani phunzilo 17 m’bulosha ya Kuphunzitsa.

  • Nkhani: (5 min. olo kucepelapo) w02 10/15 30-31—Mutu: N’cifukwa Ciani Akhristu Afunika Kukhala na Nsanje Yaumulungu? (th phunzilo 6)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 126

  • “Kodi Ndimwe Wokonzeka?”: (15 min.) Nkhani yokambidwa na mkulu. Tambitsani vidiyo yakuti Kodi Mwakonzekela Tsoka la Zacilengedwe?. Phatikizamponi zikumbutso zocokela ku ofesi yanthambi ndiponso kwa akulu, ngati zilipo.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 113

  • Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)

  • Nyimbo 84 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani