LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsa. 2
  • Yosefe Anacitilidwa Nsanje

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yosefe Anacitilidwa Nsanje
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • ‘Tamvelani Maloto Awa’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Abale Ake Amuzonda Yosefe
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 May tsa. 2
Abale ake a Yosefe akumudonsela ku citsime copanda madzi. Mmodzi wa abale ake wanyamula mkanjo wa Yosefe.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 36-37

Yosefe Anacitilidwa Nsanje

37:3-9, 11, 23, 24, 28

Zimene Yosefe anakumana nazo zionetsa kuopsa kokhala na nsanje yosayenela. Gwilizanitsani malemba na zifukwa zake zimene tiyenela kuthetsela nsanje iliyonse yosayenela.

LEMBA

  • 1 Sam. 18:8, 9

  • Miy. 14:30

  • 2 Akor. 12:20

  • Agal. 5:19-21

CIFUKWA

  • Anthu a nsanje sadzaloŵa mu Ufumu wa Mulungu

  • Nsanje imasokoneza mtendele na mgwilizano mu mpingo

  • Nsanje imavulaza kuthupi

  • Nsanje imalepheletsa kuona zabwino mwa ena

N’zocitika ziti zimene zingatipangitse kuyamba kucitila nsanje anthu ena?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani