LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • wp25 na. 1 tsa. 16
  • Kodi Munadzifunsapo Mafunso Awa?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Munadzifunsapo Mafunso Awa?
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2025
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2025
wp25 na. 1 tsa. 16
Msilikali wokhala ndi mfuti akudziyelekezela kuti ali ndi mkazi wake ndi mwana wake wamkazi akuyenda m’munda padziko lapansi lokongola komanso lamtendele.

Kodi Munadzifunsapo Mafunso Awa?

  • Popeza tonse mtendele timaufuna, n’cifukwa ciyani padziko lapansi pakucitika nkhondo zambili conci?

  • Kodi n’zothekadi kukhala ndi mtendele weniweni m’dziko lodzala ndi ciwawali?

  • Kodi nkhondo zidzathadi padzikoli?

Mungadabwe ndi mayankho amene Baibo imapeleka pa mafunso amenewa, ndipo mayankho amenewa adzakulimbikitsani.

Mungacite bwino kudziwelengela nokha zimene Baibo imakamba pa nkhani yofunika imeneyi? Magazini ino ya Nsanja ya Mlonda ingakuthandizeni kucita zimenezi.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani