LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • g19 na. 2 tsa. 16
  • Malangizo Owonjezela kwa Makolo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Malangizo Owonjezela kwa Makolo
  • Galamuka!—2019
  • Nkhani Zofanana
  • 12 Zolinga
    Galamuka!—2018
  • Thandizo Ilipo
    Galamuka!—2020
  • Tingapeze Kuti Mayankho a Mafunso Ofunika Kwambili Onena za Umoyo?
    Tingapeze Kuti Mayankho a Mafunso Ofunika Kwambili Onena za Umoyo?
  • Kodi Baibo Ingakuthandizeni Bwanji pa Umoyo Wanu?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
Onaninso Zina
Galamuka!—2019
g19 na. 2 tsa. 16

Malangizo Owonjezela Kwa Makolo

Aŵelenga Baibo

Monga mwaonela, malangizo ali m’magazini ino ni ozikidwa pa mfundo za m’Baibo. Baibo imapeleka malangizo opindulitsa kwambili kwa aliyense m’banja. Ndipo mfundo zake zimathandiza munthu kukhala woganiza bwino, komanso kupanga zosankha zanzelu.—Miyambo 1:1-4.

BAIBO IMAYANKHANSO MAFUNSO OFUNIKA KWAMBILI MU UMOYO, MONGA AKUTI:

  • ● Kodi colinga ca moyo n’ciani?

  • ● Kodi tiyenela kuimba Mulungu mlandu cifukwa ca mavuto athu?

  • ● Kodi cimacitika n’ciani munthu akamwalila?

Tikupemphani kuti mudziŵelengele mwekha Baibo, kuti mupeze mayankho pa mafunso aya na enanso. Tambani vidiyo yakuti, N’cifukwa Ciani Muyenela Kuphunzila Baibulo? yendani pa www. jw.org.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani