LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • g21 na. 1 tsa. 16
  • Kodi Mungakonde Kudziŵa Zambili?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mungakonde Kudziŵa Zambili?
  • Galamuka!—2021
  • Nkhani Zofanana
  • Nzelu Yeniyeni Imafuula
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • “Mtima Wodekha Ndiwo Moyo wa Munthu”
    Galamuka!—2020
  • Phindu la Nzelu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
Galamuka!—2021
g21 na. 1 tsa. 16

Kodi Mungakonde Kudziŵa Zambili?

Vidiyo ya mfundo zothandiza ikulila pa foni.

Munthu wina wanzelu analemba kuti: “Nzelu ndiyo cinthu cofunika kwambili. Peza nzelu, ndipo pa zinthu zonse zimene upeze, upezenso luso lomvetsa zinthu.” (Miyambo 4:7) Mlengi wathu amatiphunzitsa kuti tikhale anzelu komanso omvetsa zinthu n’colinga cakuti tizipanga zisankho zabwino na kukhala na umoyo wacimwemwe.

Kuti mudziŵe zambili zokhudza malangizo anzelu a m’Baibo, pitani pa jw.org. Pamenepo mudzapeza . . .

  • BAIBO

  • MAVIDIYO

  • MAVIDIYO A TUKADOLI

  • MBALI ZA KUFUNSA MAFUNSO

  • NKHANI

Zonsezi ni zaulele, ndipo zimathandiza anthu a misinkhu yosiyana-siyana komanso a zikhalidwe zosiyana-siyana.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani