LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 26
  • Yendani ndi Mulungu!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yendani ndi Mulungu!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Uziyenda na Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tifunika Kuphunzitsidwa
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tiziphunzitsidwa Ndi Yehova
    Imbirani Yehova
  • ‘Tsimikizilani Zinthu Zofunika Kwambili’
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 26

Nyimbo 26

Yendani ndi Mulungu!

(Mika 6:8)

1. Yendanitu ndi Mulungu;

Kondani chifundo.

Khulupirirani M’lungu;

Kuti musatope.

Mukatsatabe cho’nadi,

Simudzanyengedwa;

Azikutsogolerani

Yehova Mulungu.

2. Yendanitu mu chiyero

Musachite tchimo.

Kulaninso mwauzimu,

Yehova akondwe.

Pazinthu zonse zoyera

Ndiponso zoona,

Ganizirani zonsezi,

Dalirani M’lungu.

3. Yendanitu mowongoka,

Mudzapeza phindu.

Mudzakhala okhutira,

Zomwe ndi dalitso.

Yendanitu ndi Mulungu,

M’tamandeni ndithu.

Tidzapezatu chimwemwe,

Mu ’tumiki wake.

(Onaninso Gen. 5:24; 6:9; Afil. 4:8; 1 Tim. 6:6-8.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani