LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 27
  • Khalani ku Mbali ya Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khalani ku Mbali ya Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Ima ku Mbali ya Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ndimakondwera Kucita Cifuniro Canu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tinadzipeleka kwa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ni Moyo Wawo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 27

Nyimbo 27

Khalani ku Mbali ya Yehova

(Eksodo 32:26)

1. Kale tinalitu achisoni,

Pokhala m’chipembedzo chonyenga;

Koma tinasangalala zedi

Titamva za Ufumu.

(KOLASI)

Yenda ndi Yehova

Umunyadire.

Khala mbali yake

Sangakusiye.

Lengeza uthenga

Wamtenderewu.

Ufumu wa Khristu

Sudzatha konse.

2. Tsopano tikusangalaladi

Ndi kufesa mbewu za cho’nadi.

Dzina la Yehova kukwezadi

Limodzi ndi abale.

(KOLASI)

Yenda ndi Yehova

Umunyadire.

Khala mbali yake

Sangakusiye.

Lengeza uthenga

Wamtenderewu.

Ufumu wa Khristu

Sudzatha konse.

3. Mdyerekezi sitidzamuopa,

Ife timadalira Yehova.

Adani akhoza kuchuluka,

M’lungu ndi mphamvu yathu.

(KOLASI)

Yenda ndi Yehova

Umunyadire.

Khala mbali yake

Sangakusiye.

Lengeza uthenga

Wamtenderewu.

Ufumu wa Khristu

Sudzatha konse.

(Onaninso Sal. 94:14; Miy. 3:5, 6; Aheb. 13:5.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani