LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 51
  • Tinadzipeleka kwa Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tinadzipeleka kwa Mulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tinadzipereka kwa Mulungu!
    Imbirani Yehova
  • Yehova Alangiza Mwacikondi Kuti: “Mwana Wanga, Khala Wanzelu”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Mumamvela Bwanji?
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yehova Akutipempha Mokoma Mtima Kuti: “Mwana Wanga, Khala Wanzeru”
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 51

NYIMBO 51

Tinadzipeleka kwa Mulungu

Yopulinta

(Mateyu 16:24)

  1. 1. M’lungu watikokela ise kwa Yesu.

    Afuna kuti tim’tsatile.

    Iye wationetsa

    Kuwala kwa co’nadi.

    Lomba ise tasankha

    Kutumikila Iye.

    (KOLASI)

    Tadzipeleka kwa Atate Yehova.

    Mwa iye na Yesu tikondwela.

  2. 2. M’pemphelo ise tilonjeza Yehova,

    Kukhala okhulupilika.

    Ise timakondwela

    Kulengeza za iye,

    Na za Ufumu wake,

    Ndipo sitidzaleka.

    (KOLASI)

    Tadzipeleka kwa Atate Yehova.

    Mwa iye na Yesu tikondwela.

(Onaninso Sal. 43:3; 107:22; Yoh. 6:44.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani