LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 59
  • Tinadzipereka kwa Mulungu!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tinadzipereka kwa Mulungu!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tinadzipeleka kwa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yehova Alangiza Mwacikondi Kuti: “Mwana Wanga, Khala Wanzelu”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yehova Akutipempha Mokoma Mtima Kuti: “Mwana Wanga, Khala Wanzeru”
    Imbirani Yehova
  • Tikhale na Cikhulupililo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 59

Nyimbo 59

Tinadzipereka kwa Mulungu!

(Mateyu 16:24)

1. M’lungu wathu watikokera kwa Khristu

Kuti akhale m’busa wathu.

Cho’nadi tachipeza,

M’lungu wachibweretsa,

Ndipotu tadzikana,

Inde tikusangalala.

(KOLASI)

Ifetu tadzipereka kwa Yehova,

N’chifukwa chake tili okondwa.

2. M’pemphero tamulonjezatu Yehova

Kuti tidzamutumikira.

Tilidi okondwera

Moti tiuza ena,

Ufumu tilengeza

Dzina lake titchukitsa.

(KOLASI)

Ifetu tadzipereka kwa Yehova,

N’chifukwa chake tili okondwa.

(Onaninso Sal. 43:3; 107:22; Yoh. 6:44.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani