LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 119
  • Tikhale na Cikhulupililo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tikhale na Cikhulupililo
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tikhale ndi Chikhulupiriro
    Imbirani Yehova
  • “Tionjezeleni Cikhulupililo”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Khalani na Cikhulupililo m’Malonjezo a Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • Mwa Cikhulupililo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 119

NYIMBO 119

Tikhale na Cikhulupililo

Yopulinta

(Aheberi 10:38, 39)

  1. 1. Mwa aneneli Mulungu kale

    Anakamba na ‘nthu onse.

    Mwa mwana wake lelo akuti,

    ‘Anthu onse alape.’

    (KOLASI)

    Kuti tikapulumuke

    Na kukhala kwamuyaya,

    Tifunika kuyesetsa

    Kulimbitsa cikhulupililo.

  2. 2. Ise mokondwa timvela Yesu

    Mwa kulengeza Ufumu.

    Tilalikile molimba mtima

    Uthenga wabwinowu.

    (KOLASI)

    Kuti tikapulumuke

    Na kukhala kwamuyaya,

    Tifunika kuyesetsa

    Kulimbitsa cikhulupililo.

  3. 3. Ise sitidzabwelela m’mbuyo.

    Tidzakhalabe olimba.

    Timadalila Mulungu wathu;

    Adzatipulumutsa.

    (KOLASI)

    Kuti tikapulumuke

    Na kukhala kwamuyaya,

    Tifunika kuyesetsa

    Kulimbitsa cikhulupililo.

(Onaninso Aroma 10:10; Aef. 3:12; Aheb. 11:6; 1 Yoh. 5:4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani