LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 54
  • Tikhale ndi Chikhulupiriro

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tikhale ndi Chikhulupiriro
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tikhale na Cikhulupililo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalani na Cikhulupililo m’Malonjezo a Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • “Tionjezeleni Cikhulupililo”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Cikhulupililo Khalidwe Limene Limatithandiza Kukhala Olimba Mwauzimu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 54

Nyimbo 54

Tikhale ndi Chikhulupiriro

(Aheberi 10:38, 39)

1. Kale Mulungu ankalankhula

Kudzera mwa aneneri.

Lero kudzera mwa mwana wake

Akuti ‘lapanitu.’

(KOLASI)

Kodi chikhulupiriro chathu

N’cho’na ndi cha ntchito?

Chikakhala choterocho,

N’chimenedi chimasunga moyo.

2. Ife mokondwa timvera Yesu,

Tilalikira Ufumu.

Ndipo tilankhula mwaufulu,

Sitibisa cho’nadi.

(KOLASI)

Kodi chikhulupiriro chathu

N’cho’na ndi cha ntchito?

Chikakhala choterocho,

N’chimenedi chimasunga moyo.

3. Ndife olimba m’chikhulupiro,

Sitidzabwerera m’mbuyo.

Kaya adani atiukire,

Tidzapezabe moyo.

(KOLASI)

Kodi chikhulupiriro chathu

N’cho’na ndi cha ntchito?

Chikakhala choterocho,

N’chimenedi chimasunga moyo.

(Onaninso Aroma 10:10; Aef. 3:12; Aheb. 11:6; 1 Yoh. 5:4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani