LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 2
  • Tikuyamikani Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tikuyamikani Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tikuyamikani Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Pemphelo la Mtumiki wa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tiziyamikila Mwayi Wathu wa Pemphelo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Umoyo wa Mpainiya
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 2

Nyimbo 2

Tikuyamikani Yehova

(1 Atesalonika 5:18)

1. Tikuyamikani Yehova M’lungu,

Mumatipatsa kuwala kwanu.

Tikuyamika mwayi wa pemphero,

Kuti tinene mavuto athu.

2. Tikuyamika potumiza Yesu

Amene anagonjetsa dziko.

Tikuyamikani potithandiza

Kukwaniritsa lonjezo lathu.

3. Tikuyamika chifukwa cha mwayi

Wolalikira za dzina lanu.

Tiyamika mudzathetsa mavuto,

Madalitso anu sadzathadi.

(Onaninso Sal. 50:14; 95:2; 147:7; Akol. 3:15.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani