LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 81
  • Umoyo wa Mpainiya

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Umoyo wa Mpainiya
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Umoyo wa Mpainiya
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo ni Cozizwitsa
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 81

NYIMBO 81

Umoyo wa Mpainiya

Yopulinta

(Mlaliki 11:6)

  1. 1. Kukaca kuseni, tikali na tulo,

    Timayenda

    kulalikila anthu kulikonse.

    Timamwetulila poŵalalikila,

    Ndipo sitileka,

    ngakhale ena samvetsela.

    (KOLASI)

    Uyu ni umoyo

    umene tasankha;

    Kucita zofuna za M’lungu.

    M’dzuŵa na mu mvula

    Ise tipilila.

    Timaonetsa kuti M’lungu tim’konda.

  2. 2. Pofika m’madzulo, tikhala olema,

    Koma timakhala

    na cisangalalo mumtima

    Uyu ni umoyo ise tinasankha

    Tiyamika Yehova

    cifukwa watidalitsa.

    (KOLASI)

    Uyu ni umoyo

    umene tasankha;

    Kucita zofuna za M’lungu.

    M’dzuŵa na mu mvula

    Ise tipilila.

    Timaonetsa kuti M’lungu tim’konda.

(Onaninso Yos. 24:15; Sal. 92:2; Aroma 14:8.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani