LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 130
  • Moyo Ndi Wodabwitsa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Moyo Ndi Wodabwitsa
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Moyo ni Cozizwitsa
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Umoyo wa Mpainiya
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Umoyo wa Mpainiya
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 130

Nyimbo 130

Moyo Ndi Wodabwitsa

(Salimo 36:9)

1. Makanda onse, ndiponso mvula,

Mbewu komanso kuwala kwa dzuwa—

Ndizodabwitsa, zonse ndi mphatso.

Zimatithandiza kukhala ndi moyo.

(KOLASI)

Choncho tichitenji ndi mphatso iyi?

Tikonde Mulungu yemwe anatipatsa.

Sitingaipeze mphatsoyi patokha,

Mphatsoyi ya moyo ndi yodabwitsadi.

2. Ena ’ngasiye kulimba mtima

N’kunena kuti: ‘Kuli bwino kufa.’

Koma ifeyo sitili choncho.

Timayamikira kukhala ndi moyo.

(KOLASI)

Choncho tichitenji ndi mphatso iyi?

Tikonde anzathu amene tili nawo.

Sitingaipeze mphatsoyi patokha,

Mphatsoyi ya moyo ndi yodabwitsadi.

(Onaninso Yobu 2:9; Sal. 34:12; Mlal. 8:15; Mat. 22:37-40; Aroma 6:23.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani