LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • snnw nyimbo 140 tsa. 5
  • Umoyo wa Mpainiya

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Umoyo wa Mpainiya
  • Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Zofanana
  • Umoyo wa Mpainiya
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo ni Cozizwitsa
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw nyimbo 140 tsa. 5

Nyimbo 140

Umoyo wa Mpainiya

Yopulinta

(Mlaliki 11:6)

  1. Kukaca kuseni, tikali na tulo,

    Timayenda

    kulalikila anthu, kulikonse.

    Timamwetulila powalalikila.

    Ndipo sitileka,

    ngakhale ena samvetsela.

    (KOLASI)

    Uyu ni umoyo

    umene tasankha;

    Kucita zofuna za M’lungu.

    M’dzuŵa na mu mvula

    ise tipilila.

    Timaonetsa kuti M’lungu tim’konda.

  2. Pofika m’madzulo, tikhala olema,

    Koma timakhala

    na cisangalalo mumtima.

    Uyu ni umoyo, ise tinasankha.

    Tiyamika Yehova

    cifukwa watidalitsa.

    (KOLASI)

    Uyu ni umoyo

    umene tasankha;

    Kucita zofuna za M’lungu.

    M’dzuŵa na mu mvula

    ise tipilila.

    Timaonetsa kuti M’lungu tim’konda.

(Onaninso Yos. 24:15; Sal. 92:2; Aroma 14:8.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani