LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 31
  • Ndife Mboni za Yehova!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndife Mboni za Yehova!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Ndise Mboni za Yehova!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cuma Capadela
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cuma Capadela
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Dzina Lanu Ndimwe Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 31

Nyimbo 31

Ndife Mboni za Yehova!

(Yesaya 43:10-12)

1. Asema timilungu,

M’lungu wo’na sam’dziwa.

Ndiwamphamvuyonse

Monga tiona.

Milunguyo sidziwa

Zinthu zili m’tsogolo.

Milunguyinso si yoona

Ndipo ilibenso mboni.

(KOLASI)

Mboni za Yehovafe

Tinena mosaopa.

M’lungu wathu akalosera

Zinthu zimachitika.

2. Tilalikire dzina

La Yehova Mulungu.

Ndi Ufumu wake

Molimba mtima.

Ena amve cho’nadi

Kuti chiwamasule.

Akamalimba, adzaimba

Kutamanda nafe M’lungu.

(KOLASI)

Mboni za Yehovafe

Tinena mosaopa.

M’lungu wathu akalosera

Zinthu zimachitika.

3. Ntchito yolalikira

Za dzina la Yehova.

Imachenjezadi

Olidetsawo.

Imathandiza anthu

Kukhululukidwadi.

Imabweretsanso chimwemwe,

Ndiponso chiyembekezo.

(KOLASI)

Mboni za Yehovafe

Tinena mosaopa.

M’lungu wathu akalosera

Zinthu zimachitika.

(Onaninso Yes. 37:19; 55:11; Ezek. 3:19.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani