LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • snnw nyimbo 147 tsa. 12
  • Cuma Capadela

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Cuma Capadela
  • Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Zofanana
  • Cuma Capadela
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Dzina Lanu Ndimwe Yehova
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Kodi Mumamvela Bwanji?
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Ndimwe Mphamvu Zathu, Ciyembekezo, na Cidalilo Cathu
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw nyimbo 147 tsa. 12

Nyimbo 147

Cuma Capadela

Yopulinta

(1 Petulo 2:9)

  1. Odzozedwa na mzimu,

    Atamanda Yehova.

    Iye anaŵasankha,

    Ndipo aŵakonda.

    (KOLASI)

    Odzozedwa anu,

    Amakutamandani.

    Amakukondani,

    Amalengeza dzina lanu.

  2. Monga mtundu woyela,

    Aphunzitsa co’nadi.

    M’lungu aŵaitana

    Kucoka ku mdima.

    (KOLASI)

    Odzozedwa anu,

    Amakutamandani.

    Amakukondani,

    Amalengeza dzina lanu.

  3. Ni okhulupilika,

    Amaitana ena,

    Kuti aloŵe m’khola

    La a nkhosa zina.

    (KOLASI)

    Odzozedwa anu,

    Amakutamandani.

    Amakukondani,

    Amalengeza dzina lanu.

(Onaninso Yes. 43:20b, 21; Mal. 3:17; Akol. 1:13.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani