LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • snnw nyimbo 152 tsa. 17
  • Ndimwe Mphamvu Zathu, Ciyembekezo, na Cidalilo Cathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndimwe Mphamvu Zathu, Ciyembekezo, na Cidalilo Cathu
  • Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Zofanana
  • Ndimwe Mphamvu Zathu, Ciyembekezo, na Cidalilo Cathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Dzina Lanu Ndimwe Yehova
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Cuma Capadela
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Kodi Mumamvela Bwanji?
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw nyimbo 152 tsa. 17

Nyimbo 152

Ndimwe Mphamvu Zathu, Ciyembekezo, na Cidalilo Cathu

Yopulinta

Daunilodi

  • Mau Cabe

(Miyambo 14:26)

  1. O Yehova, munalonjeza

    za moyo wosatha.

    Tifuna kuuza ena

    za lonjezo lanu.

    Mavuto amatifoketsa,

    Tisoŵa na cocita.

    Komanso timaiŵala

    za lonjezo lanu.

    (KOLASI)

    Ise timakudalilani

    M’lungu

    kuti mudzatithandiza.

    Pamene tikulalikila anthu

    tipeza mphamvu

    mwa imwe.

  2. Tithandizeni kukumbuka

    kuti mumatikonda.

    Ngakhale timavutika,

    Simumatisiya.

    Tilalikila mosaopa

    kwa amene tapeza.

    Mumatilimbitsa mtima

    Pophunzitsa anthu.

    (KOLASI)

    Ise timakudalilani

    M’lungu

    kuti mudzatithandiza.

    Pamene tikulalikila anthu

    tipeza mphamvu

    mwa imwe.

(Onaninso Sal. 72:13,14; Miy. 3:5, 6, 26; Yer. 17:7.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani