LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 32
  • Khalani Olimba, Osasunthika

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khalani Olimba, Osasunthika
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Cilimikani, Musasunthike!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • N’dzayenda mu Umphumphu Wanga
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yendani ndi Mtima Wosagawanika
    Imbirani Yehova
Imbirani Yehova
sn nyimbo 32

Nyimbo 32

Khalani Olimba, Osasunthika

(1 Akorinto 15:58)

1. Anthu akuvutika kwambiri.

Poopa zinthu zili m’tsogolo.

Tikhale osasunthika konse,

Potumikira M’lungu.

(KOLASI)

Tikhaletu olimba

Tisiyane ndi dziko.

Tidye choonadi,tikhulupirike.

2. Misampha ndi yambiri m’dzikoli.

Koma mwanzeru tingaipewe.

Tikakhulupirira Mulungu,

Adzatisamalira.

(KOLASI)

Tikhaletu olimba

Tisiyane ndi dziko.

Tidye choonadi,tikhulupirike.

3. Tilambire Yehova Mulungu,

Tim’tumikire mogwirizana.

Tilalike uthenga mwachangu,

Mapeto adzafika.

(KOLASI)

Tikhaletu olimba

Tisiyane ndi dziko.

Tidye choonadi,tikhulupirike.

(Onaninso Luka 21:9; 1 Pet. 4:7.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani