LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 4
  • Tipange Dzina Labwino kwa Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tipange Dzina Labwino kwa Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tipange Dzina Labwino na Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Dzina la Mulungu N’ndani?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2019
  • Yehova Akweza Dzina Lake
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
  • Kugwilitsila Nchito Dzina la Mulungu ndi Kudziŵa Tanthauzo Lake
    Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 4

Nyimbo 4

Tipange Dzina Labwino kwa Mulungu

(Mlaliki 7:1)

1. Pamoyo wathu, Tsiku lililonse

Tipange dzina Labwino kwa M’lungu.

Tikachita ntchito Zabwino kwa M’lungu,

Tisangalatsa Mtima wake.

2. Kufunitsitsa Kutchuka m’dzikoli,

Kufuna kuti Anthu atikonde

Kulibetu phindu Chifukwa Yehova

Sangatikonde Tikatero.

3. Tifuna M’lungu Atilembe dzina

Kuti tikhale, Mu buku la moyo.

Choncho tikhaletu Ndi dzina labwino

Kwa M’lungu wathu, Nthawi zonse.

(Onaninso Gen. 11:4; Miy. 22:1; Mal. 3:16; Chiv. 20:15.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani