LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 11
  • Tikondweretse Mtima wa Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tikondweretse Mtima wa Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tikondweletse Mtima wa Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Mumamvela Bwanji?
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Mumamvela Bwanji?
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • “Muzitsimikizira Kuti Zinthu Zofunika Kwambiri Ndi Ziti”
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 11

Nyimbo 11

Tikondweretse Mtima wa Yehova

(Miyambo 27:11)

1. M’lungu takulonjezani,

kuchita zofuna zanu.

Tidzagwira ntchito yanu

Mtima wanu ukondwere.

2. Kapolo wanu padziko,

Amapereka chakudya

Iye amatithandiza

Kuchita zofuna zanu.

3. Mutipatse mzimu wanu,

Kuti tikhulupirike

Inde tikutamandeni,

Mtima wanu ukondwere.

(Onaninso Mat. 24:45-47; Luka 11:13; 22:42.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani