LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 42
  • “Muthandize Ofookawo”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Muthandize Ofookawo”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Thandizani Ofooka.”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Pamene Ndili Wofooka, M’pamene Ndimakhala Wamphamvu”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Kodi Mumaona Zofooka za Anthu Mmene Yehova Amazionela?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Pemphelo la Munthu Wovutika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 42

Nyimbo 42

“Muthandize Ofookawo”

(Machitidwe 20:35)

1. Tonse tili n’zofo’ka

Pamoyo wathu.

Komabetu Yehova

Amatikonda.

Iye n’ngwachifundo,

Atisamalira.

Tisonyeze chikondi

Kwa ovutika.

2. Kodi ndani safo’ka

Panthawi zina?

Khristu anatigula,

Tipeze moyo.

Ofo’ka n’nga M’lungu,

Awalimbikitsa.

Timve zovuta zawo

Tiwatonthoze.

3. Tisanyoze ofo’ka,

Tiwakumbuke

Inde, tiwasonyeze

Kukoma mtima.

Tichitedi khama,

Powalimbikitsa.

Tikawathandizadi

Atonthozedwa.

(Onaninso 2 Akor. 11:29; Yes. 35:3, 4; Agal. 6:2.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani