LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 102
  • “Thandizani Ofooka.”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Thandizani Ofooka.”
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Muthandize Ofookawo”
    Imbirani Yehova
  • Kodi Mumaona Zofooka za Anthu Mmene Yehova Amazionela?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • “Pamene Ndili Wofooka, M’pamene Ndimakhala Wamphamvu”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Khalani Wolimba!
    Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela wa 2018-2019—Wa Woimila Nthambi
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 102

NYIMBO 102

“Thandizani Ofooka.”

Yopulinta

(Machitidwe 20:35)

  1. 1. Tonse tingalakwitse

    Nthawi ‘liyonse,

    Koma Mulungu wathu

    Amatikonda.

    Iye ni cikondi;

    Ni wokoma mtima.

    Tionetse cikondi

    Kwa ovutika.

  2. 2. Tiyeni tilimbitse

    Onse ofo’ka.

    Tingaŵalimbikitse

    Mwa mau athu.

    Ni nkhosa za M’lungu

    Adzaŵalimbitsa.

    Akapeza mavuto

    Tiŵathandize.

  3. 3. Ise tisasulize

    Anthu ofo’ka.

    Tiŵaonetse

    Kuti timaŵakonda.

    Ticite mwakhama

    Poŵalimbikitsa.

    Tikaŵathandizila,

    Atonthozedwa.

(Onaninso Yes. 35:3, 4; 2 Akor. 11:29; Agal. 6:2.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani