LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 45
  • Pitani Patsogolo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pitani Patsogolo
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pita Patsogolo!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Lalikila Mau”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Ku Nyumba ndi Nyumba”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 45

Nyimbo 45

Pitani Patsogolo

(Aheberi 6:1)

1. Pita patsogolo kula mu mzimu!

Mulungu afuna tikhaledi aluso.

Sonyezatu luso muutumiki,

M’lungu adzadalitsa.

Utumikiwu ndi wa onse.

Yesu naye anauchita.

Dalira Mulungu kuti usagwe,

Limba pa chilungamo.

2. Pita patsogolo molimba mtima!

Lalika uthenga kwa anthu onse m’dziko.

Tamanda Yehova Mfumu yathuyo,

Polalikira nawo.

Adani angatiopseze.

Tisaleke, onse amvetu

Kuti Ufumu wa M’lungu wayamba.

Phunzitsa choonadi.

3. Pita patsogolo usabwerere,

Wonjezera luso ntchitoyi n’njaikulu.

Mzimu wa Mulungu ukuthandize,

Udzapeza chimwemwe.

Konda anthu omwe wapeza.

Bwerera, uwafike m’mtima.

Athandize apite patsogolo,

Cho’nadi chiziwala.

(Onaninso Afil. 1:27; 3:16; Aheb. 10:39.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani