LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 52
  • Tetezani Mtima Wanu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tetezani Mtima Wanu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Titeteze Mitima Yathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Konzekeletsani Mtima Wanu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2025
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 52

Nyimbo 52

Tetezani Mtima Wanu

(Miyambo 4:23)

1. Tetezani mtima wanu

Mukhale ndi moyo.

Mulungu adziwa bwino

Mmene tililidi.

Mtima ndi wonyenga

ungakusocheretseni.

Choncho ganizani bwino,

Mverani Yehova.

2. Konzanitu mtima wanu

Ufune Yehova

Pempherani muuzeni

Za kukhosi kwanu.

Zomwe M’lungu aphunzitsa

Tiyeni timvere,

Choncho tidzamutamanda

Tsiku lililonse.

3. Tetezani mtima wanu

Mupewe zoipa.

Akufikeni pa mtima.

Mawu a Mulungu

Yehova akonda onse

Okhulupirika.

Choncho mulambirenitu

Monga bwenzi lake.

(Onaninso Sal. 34:1; Afil. 4:8; 1 Pet. 3:4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani