LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 82
  • Tsanzirani Khristu Pokhala Anthu Ofatsa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tsanzirani Khristu Pokhala Anthu Ofatsa
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tengelani Kufatsa kwa Khristu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yesetsani Kukhala Ofatsa Kuti Mukondweletse Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Kufatsa—Kodi Khalidweli Limatipindulitsa Bwanji?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • “Bwelani kwa Ine . . . Ndipo Ndidzakutsitsimutsani”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Imbirani Yehova
sn nyimbo 82

Nyimbo 82

Tsanzirani Khristu Pokhala Anthu Ofatsa

(Mateyu 11:28-30)

1. Yesu anali woposa ’nthu onse.

Sanafune kutchuka, sananyade.

Anapatsidwa ntchito yofunika

Komabe anali wodzichepetsa.

2. Amene muli ndi mavuto nonse,

Goli lake akuti munyamule

Ndipo inu mudzatsitsimulidwa.

Ambuye wathu Yesu ndi wofatsa.

3. Anati: “Nonsenu ndinu abale.”

Musadzikweze, mutumikirane.

Ofatsa kwa M’lungu ndi ofunika,

Dziko lapansili adzalandira.

(Onaninso Mat. 5:5; 23:8; Miy. 3:34; Aroma 12:16.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani