LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 120
  • Tengelani Kufatsa kwa Khristu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tengelani Kufatsa kwa Khristu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tsanzirani Khristu Pokhala Anthu Ofatsa
    Imbirani Yehova
  • Kufatsa—Kodi Khalidweli Limatipindulitsa Bwanji?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Yesetsani Kukhala Ofatsa Kuti Mukondweletse Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Khalani Wamphamvu Pokhala Wofatsa
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 120

NYIMBO 120

Tengelani Kufatsa kwa Khristu

Yopulinta

(Mateyu 11:28-30)

  1. 1. Yesu anali wopambana m’zonse.

    Koma sananyade, sanadzikweze.

    Modzicepetsa anadzipeleka,

    Kucita cifunilo ca Yehova.

  2. 2. Olemedwa na nkhawa zosautsa,

    Adzaŵathandiza kuthetsa nkhawa.

    Ndipo iwo adzatsitsimulidwa

    Akafuna za Ufumu coyamba.

  3. 3. Yesu anati ‘se ndise abale.

    Tisadzikweze tikhale ofatsa.

    Yehova M’lungu adzatidalitsa,

    Tidzapezadi moyo wamuyaya.

(Onaninso Miy. 3:34; Mat. 5:5; 23:8; Aro. 12:16.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani