LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 67
  • Muzipemphera kwa Yehova Tsiku Lililonse

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Muzipemphera kwa Yehova Tsiku Lililonse
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pemphela kwa Yehova Tsiku na Tsiku
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mwayi Wa Pemphelo
    Zimene Baibulo Ingatiphunzitse
  • Kodi Yehova Amamvetsela kwa Ife?
    Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya
  • Muyandikileni Mulungu Kupitila m’Pemphelo
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 67

Nyimbo 67

Muzipemphera kwa Yehova Tsiku Lililonse

(1 Atesalonika 5:17)

1. Pemphera kwa Yehova amamva.

Ndi mwayi umene watipatsa.

Mu’ze zakukhosi monga mnzako,

Ndi wodalirika, bwenzi lako.

Pempherabe kwa M’lungu.

2. Pemphera kwa M’lungu uthokoze.

Um’pemphe akukhululukire.

Timuuze zakukhosi kwathu,

Amadziwa zofooka zathu.

Pempherabe kwa M’lungu.

3. Pemphera kwa M’lungu zikavuta,

Ndi Tate wathu akuthandiza.

Um’pemphe kuti akuteteze,

Um’khulupirire usaope.

Pempherabe kwa M’lungu.

(Onaninso Mat. 6:9-13; 26:41; Luka 18:1.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani