LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 109
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake
    Imbirani Yehova
  • Mafunso Ocokela Kwa Oŵelenga
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Tamandani Mfumu Yatsopano ya Dziko Lapansi
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 109

Nyimbo 109

Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!

(Aheberi 1:6)

1. Tamandani Yesu

Mfumu yodzozedwayo.

Yokonda choonadi

Komanso chilungamo.

Popereka ulemu

Ku dzina la M’lungu,

Ulamuliro wake

Adzalengezatu.

(KOLASI)

Tamandani Yesu!

Wodzozedwa wa M’lungu.

Anakhazikitsidwa

Pampando monga Mfumu!

2. Tamandani Yesu

Yemwe anatifera.

Anapereka dipo.

Ndithu n’ngodzichepetsa.

Mkwatibwi wake pano

Akudikirira.

Ukwati n’ngwakumwamba

Udzatidalitsa.

(KOLASI)

Tamandani Yesu!

Wodzozedwa wa M’lungu.

Anakhazikitsidwa

Pampando monga Mfumu!

(Onaninso Sal. 2:6; 45:3; Chiv. 19:8.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani