LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 85
  • Mphoto Yaikulu Yochokera Kwa Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mphoto Yaikulu Yochokera Kwa Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova “Akufupe Mokwanila”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kutumikila Yehova na Moyo Wonse
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata
    Imbirani Yehova
  • Tizitumikira Yehova ndi Moyo Wathu Wonse
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 85

Nyimbo 85

Mphoto Yaikulu Yochokera Kwa Yehova

(Mateyu 19:29)

1. Yehova amadziwa anthu onse

Omwe amam’tumikira.

Amadziwa kuti pa nthawi zina

Zinthu zina ’mamanidwa.

Ngati mwasiya abale ndi nyumba

M’lungu akudziwa bwino.

Amatipatsa ’bale auzimu

Ndi moyo m’paradaiso.

(KOLASI)

Yehova wotonthoza aone

Ndiponso akupatseni mphoto.

Bisalani m’mapiko ake,

N’ngokhulupirika, Iye n’ngwabwino.

2. Mwina n’kusankha kwawo mwina ayi

Kuti ena sali m’banja.

Akamafuna Ufumu wa M’lungu

Iwo amadalitsidwa.

Amasungulumwatu nthawi zina,

Zimenezi tikudziwa.

Monga abale ndi alongo awo

Tikhale olimbikitsa.

(KOLASI)

Yehova wotonthoza aone

Ndiponso akupatseni mphoto.

Bisalani m’mapiko ake,

N’ngokhulupirika, Iye n’ngwabwino.

(Onaninso Ower. 11:38-40; Rute 2:12; Mat. 19:12.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani