LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 41
  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Lambila Yehova Ukali Wacicepele
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ubwino
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Bwerani Mudzatsitsimulidwe!
    Imbirani Yehova
  • Yehova “Akufupe Mokwanila”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 41

Nyimbo 41

Lambirani Yehova Muli Achinyamata

(Mlaliki 12:1)

1. Anyamata ndi atsikananu,

Ndinu ofunika kwa Mulungu.

Iye amakukondani zedi

Kudzeratu mwa makolo anu.

2. Lemekezani makolo anu,

Ndipo musapikisane nawo.

M’kakondedwa ndi anthu ndi M’lungu,

Mudzakondwera ndi unyamata.

3. Kumbukira Mlengi mu’nyamata

Uzikonda cho’nadi kwambiri.

Ukadzipereka kwa Yehova,

Iye ndithudi adzakondwera.

(Onaninso Sal. 71:17; Maliro 3:27; Aef. 6:1-3.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani