LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 119
  • Bwerani Mudzatsitsimulidwe!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Bwerani Mudzatsitsimulidwe!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Bwelani Mutsitsimulidwe!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Tikhale na Cikhulupililo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 119

Nyimbo 119

Bwerani Mudzatsitsimulidwe!

(Aheberi 10:24, 25)

1. Tikukhaladi m’dziko losochera,

Anthu sakudziwa M’lungu.

Tikufunikiradi malangizo

Osonyeza njira yathu.

Misonkhano yathu imathandiza

Kukhala n’chiyembekezo,

Imatilimbikitsa n’kutipatsa

Mphamvu yochita zabwino.

Zimene Yehova watilamula

Ife sitidzazisiya.

Pamisonkhano yathu timapeza

Malangizo oyenera.

2. Yehova akudziwa bwino zinthu

Zomwe timafunikira.

Tikamasonkhana timasonyeza

Kuti timamudalira.

Tikamamvera nkhani za abale

Timalimbikitsidwadi.

Timadziwa kuti sitili tokha,

Iwo atithandizadi.

Poyembekezera Paradaiso

Sitisiya kusonkhana.

Tiziphunzira kugwiritsa ntchito

Nzeru yochoka kumwamba.

(Onaninso Sal. 37:18; 140:1; Miy. 18:1; Aef. 5:16; Yak. 3:17.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani