LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 53
  • Kukonzeka Kukalalikila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kukonzeka Kukalalikila
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kukonzeka Kukalalikila
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Phunzilo 3
    Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
  • ‘Ine Nilipo, N’tumizeni!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Ine Ndilipo! Nditumizeni”
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 53

NYIMBO 53

Kukonzeka Kukalalikila

Yopulinta

(Yeremiya 1:17)

  1. 1. N’kuseni,

    Tikonzeke

    Kupita mu‘tumiki.

    Mvula ikugwa,

    Ndipo kwazizila.

    Tingafune kupitiliza

    kugona.

    (KOLASI)

    Pemphelo na kukonzekela,

    Izi tikacita;

    Tidzalalikila uthenga,

    Mosaleka.

    Angelo amatithandiza.

    Yesu aŵatuma.

    Na bwenzi lokhulupilika,

    Sitifo’ka.

  2. 2. Cimwemwe

    Tidzapeza

    Ngati tipitiliza.

    Ndipo tidziŵa

    Kuti M’lungu wathu,

    Amaona zonse zimene

    ticita.

    (KOLASI)

    Pemphelo na kukonzekela,

    Izi tikacita;

    Tidzalalikila uthenga,

    Mosaleka.

    Angelo amatithandiza.

    Yesu aŵatuma.

    Na bwenzi lokhulupilika,

    Sitifo’ka.

(Onaninso Mlal. 11:4; Mat. 10:5, 7; Luka 10:1; Tito 2:14.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani